» 
 » 
Malawi Native Anthem Text



Unknown - Malawi Native Anthem Text - Текст песни

1.

Mlungu dalitsani Malawi,

Mumsunge m'mtendere.

Gonjetsani adani onse,

Njala, nthenda, nsanje.

Lunzitsani mitima yathu,

Kuti tisaope.

Mdalitse Mtsogo leri na fe,

Ndi Mai Malawi.

2.

Malawi ndziko lokongola,

La chonde ndi ufulu,

Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri,

Ndithudi tadala.

Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,

N'mphatso zaulere.

Nkhalango, madambo abwino.

Ngwokoma Malawi.

3.

O! Ufulu tigwirizane,

Kukweza Malawi.

Ndi chikondi, khama, kumvera,

Timutumikire.

Pa nkhondo nkana pa mtendere,

Cholinga n'chimodzi.

Mai, bambo, tidzipereke,

Pokweza Malawi.

Sent by Carlos AndrГ© Pereira da Silva Branco   
Другие материалы по этой песне:
  • Текст (слова)

https://primanota.net/unknown/malawi-native-anthem-text-lyrics.htm